Bemba
First Verse
Lumbanyeni Zambia, no kwanga,
Ne cilumba twange tuumfwane,
Mpalume sha bulwi bwa cine,
Twaliilubula.
Twikatane bonse.
Second Verse
Bonse tuli bana ba Africa,
Uwasenaminwa na Lesa,
Nomba bonse twendele pamo,
Twaliilubula.
Twikatane bonse.
Third Verse
Fwe lukuta lwa Zambia lonse,
Twikatane tubyo mutende,
Pamo nga lubambe mu mulu,
Lumbanyeni Zambia.
Twikatane bonse.
Chorus (Mostly Sung After First Verse)
Lumbanyeni,
Lesa, Lesa, wesu,
Apale calo,
Zambia, Zambia, Zambia.
Fwe bantungwa
Mu luunga lwa calo.
Lumbanyeni Zambia.
Twikatane bonse.
Chewa
First Verse
Imani timtamande Zambia,
Dziko la cimwemwe ndi umodzi,
Ife tinamenyera ufulu,
Tinapata ufuluwu,
Umodzi ndi mphamvu.
Second Verse
Africa ndiye Mayi wathu,
Dzanja la Mbuye lamdalitsa
Tiyeni tonse tigwirizane
Ndife abale m’dziko:
Umodzi ndi mphamvu.
Third Verse
Dziko limodzi, mtundu umodzi
Ndi cilakolako cathutu
Ulemu ndi mtendere m’dziko
Monga nkwazi m’mwamba:
Umodzi ndi mphamvu.
Chorus (Mostly Sung After First Verse)
Timtamande,
Mlungu, Mlungu wathu,
Adalitse,
Zambia, Zambia, Zambia.
Omasuka pansi
Pa ndembela yathu.
Zambia timtamande.
Umodzi ndi mphamvu.
Tonga
First Verse
Atumutembaule Zambia,
mbotubelekela antoomwe,
Twakazunda akwaanguluka,
Akulilela,
Toonse Tuswangane.
Second Verse
Afrika mbabaama besu,
Cisi cakalelekw’ aLeza,
Toonse tobantu tuswaangane,
Mubwanabokwabo,
Zambia Omubotu.
Third Verse
Ciinga comwe ncotulilila,
Mbulemu aluumuno mucisi,
Mbuli Sikwaze Mbwauluka,
Zambia, omubotu,
Toonse Tuswangane.
Chorus (Mostly Sung After First Verse)
Ciinga comwe ncotulilila,
Mbulemu aluumuno mucisi,
Mbuli Sikwaze Mbwauluka,
Zambia, omubotu,
Toonse Tuswangane.
English
First Verse
Stand and sing of Zambia, proud and free,
Land of work and joy in unity,
Victors in the struggle for our rights,
We’ve won freedom’s fight.
All one, Strong and Free.
Second Verse
Africa is our own motherland,
Fashion’d with and blessed by God’s good hand,
Let us all her people join as one,
Brothers under the sun.
All one, Strong and Free.
Third Verse
One land and one nation is our cry,
Dignity and peace ‘neath Zambia’s sky,
Like our noble eagle in its flight,
Zambia, praise to thee.
All one, Strong and Free.
Chorus (Mostly Sung After First Verse)
Praise be to God,
Praise be, praise be, praise be,
Bless our great nation,
Zambia, Zambia, Zambia.
Free men we stand
Under the flag of our land.
Zambia, praise to thee!
All one, Strong and Free.